Pusha-music

25/01/2025

Mwati zakhala bwanji zaa anthu obwela KU America ๐Ÿ‡บ๐Ÿ‡ธ ๐Ÿ™„๐Ÿ™„๐Ÿ™„

Breaking news South Africa Pretoria mzimayi amene mukumuonayi  waphedwa usiku wapa 22 January ma report ak*t mamunayi mu...
24/01/2025

Breaking news South Africa Pretoria mzimayi amene mukumuonayi waphedwa usiku wapa 22 January ma report ak*t mamunayi mukumuonayi anali ndibanja lake ndipo banjalo linasokonekela ndipo litasokonekela njondayi Inapeza chibwezi china ndipo ubwezi wawo ukuyenda mzimayi wina ananyamuka kukamuuza mnkazi oosyidwayo k*t mamuna wako amayenda ndiwak*t ndipo panopa alimodzi ndipo mzimayi osiyidwa banjayo sanachedwe ndikunyamula mpeni ndipo atafika kunyumba kwazakeyo anapeze alipachikondi chazaonene ndipo sanachedwe ndikuyiyambitsa ndewu mosakhalitsa anabaya mzakeyo muthiti kenako ndikubayaso njondayo pakhosi sipanadutse kathawi winayo kumwalila ndipo mtolankhani wathu wati mzimayi opha mzakeyo pomwepo watoledwa ndi a police malemuwa amachoke m.boma la magochi report by @ wilad usufu

23/01/2025

: Moto wolusa womwe ukukula mwachangu wabuka m'mapiri kumpoto kwa Los Angeles m'dziko la America.

Ndipo anthu oposa 50,000 okhala mโ€™chigawo cha California achenjezedwa k*ti achoke mโ€™nyumba zawo k*tsatira kubuka kwa motowu.

Pakanali pano motowu womwe wabuka pafupi ndi nyanja ya Castaic waononga kale mahekitala okwana 3,750 m'maola ochepa chabe.

19/01/2025

BREAKING: TikTok says it will restore service to U.S. users after assurance from President-elect Trump to the companyโ€™s service providers.

Just hours before the move from TikTok, Trump posted to Truth Social calling for the app to remain available. Trump indicated in his post that he wanted it to be available in order to broadcast his inauguration Monday.

NKHANI YONVETSA CHISONI YOMWE INA NDICHITIKIRA ANANDILUMIKIZITSA KUZIDOLO KOMA M'MATSENGA.Dzina langa ndi innocent saona...
19/01/2025

NKHANI YONVETSA CHISONI YOMWE INA NDICHITIKIRA ANANDILUMIKIZITSA KUZIDOLO KOMA M'MATSENGA.

Dzina langa ndi innocent saona

Kungoyambira pachinyamata changa, moyo wanga wakhala osanvetsetseka malingana ndizomwe ndakhala ndikukumana nazo.

Ndimati ndikapeza kachibwezi, sindimatha chaka chisanathepo koma ine osalakwa.

Nthawi zambiri ndimakhala ndikukhumudwitsidwa koma vuto langa osalipeza.

Mpaka ndinafika pongo giver basi k*ti mwina zazibwezi simbali yathu. Zinalibe zovuta pauchinyamata kukhala opanda wachikondi.

Ma friends ndi anthu ena okuzungulira nkhani imakhala yanga Komabe nanga ndidakatani popeza ndimakhalira kukhumudwitsidwa.

Ndinakula mpaka 30 years koma opanda mkazi. Ndinakhala pafupifupi kwazaka 5 osaipeza ntchito.

Chirichonse sichimandiyendera ndipo ndimangosowa mtendere ndikamakhala nkumazifusa k*ti kwenikweni ine vuto ndichani?

Ndinapeza ntchito mwamwayi yomasesa komanso kukolopa ku restaurant ndipo ndinalidi ozipereka ndipo ndimailemekeza ntchito yanga. Ngakhale ndinali okhulupirika koma salary yanga samandikwezera pamene ena amawakwezera.

Pena mpaka ndimatha myezi iwiri osalandira, moti ndimalephera kungoisiya ntchitoyo k*ti nanga ndikaisiya ndilowera k*tiko???

Tsiku lina ndikusesa ndinaona munthu wina wabambo atakhala pa mpando akundikodola. Bamboyo amandiitanira chakudya k*ti tidye limodzi. Ndinayesesa kukana koma anakakamira ndithu mpaka ndinayambadi kudya naye.

Koma tirinkati mokudya muja, adandilakhula nk*ti chifukwa chani ndikuoneka osowa mtendere ndiwankhawa? Ine misozi inayamba kugwa ๐Ÿ˜ญ๐Ÿ˜ญ๐Ÿ˜ญ ndikuchita kusowa poyamba kuyakhira.

Ndirinkati mozinvera chisoni muja, bamboyo adangondiuza k*ti lero ndikaweruka kuntchito ndingopita direct kunyumba kwanga ndipo ndizikapephera mpaka nthawi yoti ndigone ikakwane.

Atangolakhula choncho bamboyo adachokapo ndipo sindithaso kumuona komwe adalowera. Nthawi yowerukira itakwana, ndinayendadi direct wapakhomo panga.

Nditafika ndinayambadi kupephera mosweka mtima poona nyengo zowawitsa zomwe ndimadutsamo. Koma zoopsa ndithu zomwe ndidaziona ndiri nkati mopephera.

Ndidangonva chithu phiii kumbuyo kwanga, pompo ndidaimirira ndikuyang'ana. Ndinaonapo zidole ziwiri zitamangidwa ndi chanet cha green.

Pompo mtima wanga udachita mantha, koma ndirinkati mochita mantha momwemo, ndidanva kulakhula pa mtima panga k*ti usaope ndipo tenga lezala udule chingwe cha net cho.

Pompo ndinatenga lezala lija ndikudula, ndinazitenga zidolezo ndichingwecho kukazitaiya nchumbudzi. M'ma k*tacha ndinakonzeka bwinobwino ulendo waku ntchito.

Nditafika ndingoitaniridwa ku office ya abwana k*ti akundifuna.

Nditafikako ndinali odabwa abwana anga akundipepesa pazonse akhala akundilakwira ngati kusandipatsa malipiro anga. Adawerenga salary yanga yonse yomwe akhala asakundipatsa ndipo idakwana Mwk250,000. Pompo andandionjezerapo Mwk500,000 ngati chipepeso yonse kukhala ngati Mwk750,000. Ntchito adandikwezanso nandipanga kukhala oyang'anira ogwira ntchito onse pa restaurant po komanso adali ndikampani ina yomwe adandinyemerakonso kaudindo.

Anandipasanso nyumba yoti ndizikhaliramo.

Ndidamuona Mulungu akukhala kumbali yanga ndipo ndidakumbukira nkulu amene adandithandiza nzeru k*ti Mulungu yekha amutsogolele.

M'bale nk*theka nawenso nyengo zako pano ziri pa zero. Wakhala ukuyang'ana ntchito ndipo sukuipeza, wakhala ukuyang'ana mwamuna/mkazi wa serious koma nthawi zonse umangokhala okhumudwitsidwa. Umadwala nthenda zamg'onamg'ona ndipo wakhala ukuyenda malo osiyanasiyana koma palibe ndichimodzi chomwe chikukuyendera.

Leronso ndikulakhula ndi moyo wako k*ti gwada pansi ndipo nyengo yako iliyonse umusiyire Mulungu. Iye aliokonzeka kuyakha nyengo zako ndipo palibe chirichonse chimene Chingamulake.

Kaya unaikidwa m'boloto, kaya unanenereredwa za moyo wako k*ti sudzakhala pantchito, sudzakhala ndi mwana, sudzakhala ndi banja, sudzapita chitsogolo lero ndik*ti back to sender mudzina la Yesu!!!
Aliyense amene adakulumikizitsa kuzidole nakumanga lero akuyenera kulandira moto wake wa Mulungu ndipo maunyolo onse ndik*ti aduke mudzina la Yesu.

Khulupirira m'bale lero k*ti Mulungu asitha nyengo zako ndipo tangokhulupirira mwa Yehovah.
Mokupepha, mdalitse wina wake lero ndi uthenga omweu popanga share kuma group 5 okha omwe ulinawo.

Pangani Follow tsambali k*ti muzitha kulandira nkhani ngati izi zomwe zizisitha nyengo zanu konse komwe muliko.

God bless you my brothers and sisters ๐Ÿ™๐Ÿ™๐Ÿ™

15/01/2025

Kod mukudziwa k*ti m***a kupanga upload music yanu mwaule pa website yathu zoyenela kuchita pangani follow this page k*ti nanu mupindule pa music yanu osamagosunga nyimbo ayi yakho lanu lapezeka https://www.facebook.com/share/1Q4QvCiwYK/

13/01/2025

With Nkhoma Synod Radio โ€“ I just got recognized as one of their top fans!

12/01/2025

Tidziwe mbili ya Coca-Cola The Coca-Cola Company is a publicly-traded company, listed on the New York Stock Exchange (NYSE) under the ticker symbol KO. As a result, there is no single individual or entity that owns the company.

Instead, The Coca-Cola Company is owned by its shareholders, who collectively hold shares of the company's stock. The largest shareholders of The Coca-Cola Company include institutional investors such as The Vanguard Group, BlackRock, and State Street Global Advisors, as well as individual investors such as Warren Buffett's Berkshire Hathaway.

The company's largest individual shareholder is Roberto Goizueta's estate, which holds approximately 3.6% of the company's outstanding shares. Roberto Goizueta was a former CEO of The Coca-Cola Company who led the company from 1981 until his death in 1997.

Here is a rough breakdown of the ownership structure of The Coca-Cola Company:

- Institutional investors: 65-70%
- Individual investors: 30-35%
- Insider ownership (employees and directors): 1-2%

Note that the ownership structure of The Coca-Cola Company may change over time due to the buying and selling of shares by its shareholders. Next The Coca-Cola Company is a publicly-traded company, listed on the New York Stock Exchange (NYSE) under the ticker symbol KO. As a result, there is no single individual or entity that owns the company.

Instead, The Coca-Cola Company is owned by its shareholders, who collectively hold shares of the company's stock. The largest shareholders of The Coca-Cola Company include institutional investors such as The Vanguard Group, BlackRock, and State Street Global Advisors, as well as individual investors such as Warren Buffett's Berkshire Hathaway.

The company's largest individual shareholder is Roberto Goizueta's estate, which holds approximately 3.6% of the company's outstanding shares. Roberto Goizueta was a former CEO of The Coca-Cola Company who led the company from 1981 until his death in 1997.

Here

11/01/2025

Congratulations Gabadinho Mhango money of much

09/01/2025
05/01/2025

The International Monetary Fund has warned that undisclosed public debt, estimated at $1 trillion globally, poses a growing threat to economic growth in low-income nations already grappling with mounting fiscal challenges.

05/01/2025

In recent years, occasions large and small โ€” parties, Super Bowls, mixed martial arts fights, even Thanksgiving โ€” have provided a reason for residents across Hawaii to set off illegal fireworks.

The increasingly sophisticated displays, loved by some and loathed by others, are so prevalent that some people consider them part of the state's culture. They have rattled neighborhoods of tightly packed houses, started fires, terrorized pets and knocked a light fixture off the ceiling of an Associated Press reporter's home, where it narrowly missed a child and shattered on the floor.

05/01/2025

The Kano State Censorship Board has suspended a popular Kannywood actress, Samha Inuwa, from appearing in films for one year due to allegations of indecent dressing.

04/01/2025

The Malawi Electoral Commission is inviting the following listed persons to report to the following Nerve Centres in the morning of 7th January 2025 For Supplementary Voter Registration in the Councils Indicated below.

You can access the full list through the following link: https://drive.google.com/file/d/13gf6azQ1He4-7NRCiJzLPJ_jV9YiR3T3/view?usp=drivesdk

For more details and enquiries regarding this exercise contact the following:

โ€ข Ellen Kulujili (Mrs) 0 999 365 633
โ€ข Maurice Manchichi 0 888 504 221
โ€ข Joshua Thanganyika 0 995 101 20


04/01/2025



A Emmanuel Phiri a zaka 26, ali mchitokosi cha a polisi ku Kasungu, komwe akuganiziridwa k*ti anaba njinga ya moto kwa Suza m'bomali.

Wachiwiri kwa wofalitsa nkhani za apolisi m'bomali, a Miracle Hauli wati pa 19 December chaka chatha, mwini njingayi yemwe ndi wa kabaza, anakadandaula ku posli k*ti njinga yake yasowa.

Apolisi atamva za nkhaniyi, anayamba kafukufuku ndipo anakwanitsa kunjata woganiziridwayu atamupeza ak*tsatsa malonda njingayi.

A Phiri, omwe amachokera m'mudzi mwa Chisi, mfumu yaikulu Tengani m'boma la Nsanje akaonekera ku bwalo la milandu posachedwapo komwe akayenkhe mlandu wakuba.

Wolemba: Nelson Gonjani.

๐๐จ๐ฅ๐ข๐œ๐ž ๐š๐ซ๐ซ๐ž๐ฌ๐ญ ๐ฌ๐ฎ๐ฌ๐ฉ๐ž๐œ๐ญ๐ž๐ ๐ค๐ข๐๐ง๐š๐ฉ๐ฉ๐ž๐ซ, ๐ซ๐ž๐ฌ๐œ๐ฎ๐ž ๐ญ๐ฐ๐จ-๐ฒ๐ž๐š๐ซ-๐จ๐ฅ๐ ๐ฏ๐ข๐œ๐ญ๐ข๐ฆThe Kano State Police Command has successfully arrested a 2...
04/01/2025

๐๐จ๐ฅ๐ข๐œ๐ž ๐š๐ซ๐ซ๐ž๐ฌ๐ญ ๐ฌ๐ฎ๐ฌ๐ฉ๐ž๐œ๐ญ๐ž๐ ๐ค๐ข๐๐ง๐š๐ฉ๐ฉ๐ž๐ซ, ๐ซ๐ž๐ฌ๐œ๐ฎ๐ž ๐ญ๐ฐ๐จ-๐ฒ๐ž๐š๐ซ-๐จ๐ฅ๐ ๐ฏ๐ข๐œ๐ญ๐ข๐ฆ

The Kano State Police Command has successfully arrested a 25-year-old suspected kidnapper, Abubakar Musa, from Rijiyar Lemo Quarters, Kano.

The Kano State Police Command has successfully arrested a 25-year-old suspected kidnapper, Abubakar Musa, from Rijiyar Lemo Quarters, Kano.

Address

Mchinji
Salima
01

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Pusha-music posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Business

Send a message to Pusha-music:

Videos

Share

Category