Amayi amene anakana 500 thousand aja anachitidwa interview dzulo ndipo anenetsa zoti ndalamayo anayikanadi ati mpakana amkachita kuwanyengelera mpaka anayikana ndalamayi katatu konse, ngati Yudas.
Izi zikutanthauza kuti zoti amayiwa anayimba phone kuti asintha maganizo zikhoza kukhala zabodza ndithu.
Umu ndi mmene zinalili mwemwe atamumanga uku akupanga demand ndalama. Ndendende ngati achina Boko Haram agwira munthu
Amayi awa tiwatengere ku khoti akafotokoze zikuoneka ngati ali ndi umboni๐. Nanga inu nanu a Brian Banda masten mwawafunsa funso nokha nanga chowakanizilanso kuyankha ndi chani?๐
Anthu ena akuti Sho Madjozi anachita kulembeledwa free style yapa Made On Monday. Chifukwa nde sizoonatu. Kuchita kumposa Charisma ๐ญ
Anthu ena akuti Bakili Muluzi Tv ndi uyuyu akamunyamule ndipo asachedwechedwe. Koma akangomunyamula ma audios ena samachedwatu. Amakhala ma audios akutuluka munthu ali ku selo๐.
Nde muli intelligence eeh nde chikadzati "akulu akulu! Thomas Sankala anatha 3 days"? Nde nde nde Bakili Muluzi TV ๐๐
#Chinsapo
Anthu atanyamula bokosi akukuwa kuti mwana wathu mutibwenzere
Wanjinga iwe watiswa mtima๐ญ๐ญ
Anthu 26 onse apita. Zovetsa chisoni. Zomwe zachitika ku Kasungu!!!๐ญ๐ญ๐ญ๐๐๐๐
Lulu kutenga microphone ๐ค mkuika mu boxer ku show ya Yo Maps. Kenako oyimba amzake anatenga mkuika kukamwa ayi zikomo๐ญ
Mau osaiwalika omwe anayankhula Dr Saulos Klaus Chilima! May God be with his family.
Rip ๐ญ๐๐ญ๐ญ
Akutitu anthu ndi asilikali akungoyenda mu nseu alibe zinthu zopangira Search. UTM team has joined the search. Why Malawi olo ndika drone komwe?
Ma video opatsa mantha ayamba kutuluka๐๐๐๐. Ati kumene ndege yagwera. #Chilima #Ndege #flight #Malawi #vicepresedent #chikangawa
Jetu analira mokweza atamuwona mwana wake patadutsa zaka 14 ali ku joni ๐โโ๏ธ๐โโ๏ธ๐โโ๏ธ. Kuyesa kumuchemelera kuti asalire kwambiri