Golden City Tower

Golden City Tower Golden City Tower is a media and entertainment company
(4)

Akutitu 7/02/2025 mmmhu  mwinatu akufuna ayankhe  uyu, a Malawi amzanga ingosungani ma bundle kumeneko
03/02/2025

Akutitu 7/02/2025 mmmhu mwinatu akufuna ayankhe uyu, a Malawi amzanga ingosungani ma bundle kumeneko

Namondwe FAIDA 🙌🏾 Nkuyesa nanu mukudzifusa kuti kodi anthuwa mayinawa amawatenga kuti ? Nanga mpaka namondwe Faida? Ndek...
03/02/2025

Namondwe FAIDA 🙌🏾

Nkuyesa nanu mukudzifusa kuti kodi anthuwa mayinawa amawatenga kuti ? Nanga mpaka namondwe Faida? Ndekutitu namondwe uyu ndiwamkazi

Bwana Jomo agula iPhone. Chimwemwe kusefukira paliponse
03/02/2025

Bwana Jomo agula iPhone. Chimwemwe kusefukira paliponse

Madam anga sanali mbulanda anavala dress lowonekera mkati says Kanye west
03/02/2025

Madam anga sanali mbulanda anavala dress lowonekera mkati says Kanye west

Happy birthday Aid fest🥳🥳
31/01/2025

Happy birthday Aid fest🥳🥳

chidzukulu cha JETU, Dyokhwe Mw  akuti zopeleka fanta kwa alendo komaso kuwaphikira nyama akamabwera ndi zausilu.Izi wan...
31/01/2025

chidzukulu cha JETU, Dyokhwe Mw akuti zopeleka fanta kwa alendo komaso kuwaphikira nyama akamabwera ndi zausilu.

Izi wanena mu nyimbo yake yomwe watulusa lero .

https://m.youtube.com/watch?v=q-iRGZhlxCw

Ma vendor Ku Blantyre alusa pamene sadapatsidwe chimanga chomwe analonjezedwa kupasidwa .
30/01/2025

Ma vendor Ku Blantyre alusa pamene sadapatsidwe chimanga chomwe analonjezedwa kupasidwa .

Oimba owuleza mtima komaso waluso .Congratulations ELI Njuchi
30/01/2025

Oimba owuleza mtima komaso waluso .
Congratulations ELI Njuchi

Kwachema ndiku twitter  pamene ma Presdent  awiri akukangana ,Ali Ku right yo ndi presdent wa Ku South Africa and winayo...
30/01/2025

Kwachema ndiku twitter pamene ma Presdent awiri akukangana ,Ali Ku right yo ndi presdent wa Ku South Africa and winayo ndi wa Ku Rwanda.
Mkanganowu ukuchitika kamba kakuphedwa ka asilikali ena aku South Africa ndi gulu la M23.

Amalawi Ali Ku ma stand kuyan'anila nkhonyayi🙌🏾

Deniss Imaan Posted Last night, as I went to bed, I was reflecting on the 2 stop-work orders in 2 WhatsApp groups I am i...
29/01/2025

Deniss Imaan Posted

Last night, as I went to bed, I was reflecting on the 2 stop-work orders in 2 WhatsApp groups I am in. These were 2 of the biggest projects I would be working on this year. I had declared my 2025 done as of last year. Now, from nowhere, out of thin air, all 'momentarily' vanished like that. I was comforting myself that I had not started drawing any funds from the projects yet, but they were promising projects.

Although I did not make commitments financially depending on these, I had put my mind at ease and started clearing some of my current obligations with other clients to focus solely on these. But yesterday, I went to sleep with none of them. If I, who was just working on a promise, with a contract in place for 1, am affected this much, how about those whose work for years now depended on USAID? I started feeling sorry for people who may lose their jobs due to this order. But it was at this moment that I realized that I am looking at this situation driven by selfish and personal gains, not the impact the people who give the money want it for. In the 2 hours I thought about this situation, never did I think of people in rural areas whose lives depend on medicines, agricultural inputs, sexual reproductive health care, critical medical supplies made available by support from The People of America. I was just thinking about what I stand to lose from my benefits and those who will lose their jobs.

This opened me to realize that I am not too far from politicians. Everyone thinks of themselves and not the people. We are all just selfish beings using other people's misery to enrich ourselves. We just want to be seen like we care, while the vulnerable watch us and think we really have their welfare at heart. We live in a sad world. I hope we can wake up and let each go fetch for themselves now without using the poor as our bait.

This experience has taught me to be more selfless and think of the greater good. I am inspired to make a positive impact on my community and the world at large. I believe that we all have the power to create change and make a difference. Let us all strive to be more empathetic and compassionate towards others. We can create a brighter future for ourselves and generations to come.

Ku Ndirande kwenikweni mukuti ndichani?Basitu anthu apeza bokosili lili panja ,atalitsegula apeza mulibe kanthu ,basitu ...
28/01/2025

Ku Ndirande kwenikweni mukuti ndichani?

Basitu anthu apeza bokosili lili panja ,atalitsegula apeza mulibe kanthu ,basitu kenaka aliwotcha

Mmmmm kunjaku sikulibwino🙌🏾

Tamia ja ndi lawyer wake.All the best Tamia
27/01/2025

Tamia ja ndi lawyer wake.

All the best Tamia

Akutitu ma hit amatulutsa ndi Kineo .Inu izi mukukhulupilira?
27/01/2025

Akutitu ma hit amatulutsa ndi Kineo .

Inu izi mukukhulupilira?

Sungani ma bundle JEG Tellem  madzulo ano ali ndizoti atiwonetse Chimadziwa kuimba ichi🙌🏾
27/01/2025

Sungani ma bundle JEG Tellem madzulo ano ali ndizoti atiwonetse

Chimadziwa kuimba ichi🙌🏾

Back again in the music industry, katswili wathu wa dancehall yemwe tinkamudalila  Malawi muno , purpose yemwe dzina lak...
26/01/2025

Back again in the music industry, katswili wathu wa dancehall yemwe tinkamudalila Malawi muno , purpose yemwe dzina lake loimbila ndi Purple C, wanena zakubwelanso kwake mu music industry ndipo akhala akutulutsa nyimbo zosiyanasiyana mmasiku ali nkudzawa.

Purple C wanena izi pa tsamba lake la mchezo kuti wabwelelaso mu music industry

Zokhudza kwambiri kuti asilikali otetezela dziko lathu atatu atisiya komwe Ku DRC ndigulu la M23May their souls rest in ...
26/01/2025

Zokhudza kwambiri kuti asilikali otetezela dziko lathu atatu atisiya komwe Ku DRC ndigulu la M23

May their souls rest in peace🕊

🚨 History in the Making: Elon Musk Crowned the Wealthiest Person of All Time!Move over, Mansa Musa! Elon Musk has shatte...
25/01/2025

🚨 History in the Making: Elon Musk Crowned the Wealthiest Person of All Time!

Move over, Mansa Musa! Elon Musk has shattered records to become the richest individual in history, amassing a jaw-dropping net worth of $436 billion. For perspective, the legendary African king Mansa Musa, who reigned during the 14th century, was estimated to have a wealth of $400 billion.

But Musk's wealth doesn't stop at breaking historical benchmarks. If you compare his fortune to global economies, he's now richer than 150 countries by GDP—yes, entire nations! To top it off, Musk's wealth surpasses the combined GDP of every single country in Africa.

The SpaceX and Tesla magnate is proving that the sky (or perhaps Mars) is the limit when it comes to building an empire.

Address

Box 20664 Mzuzu
Mzuzu

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Golden City Tower posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Business

Send a message to Golden City Tower:

Videos

Share