
02/10/2025
Lero pa 2 October ndi tsiku limene m'busa Masona Kaluluma Tembo wa mu mpingo wa CCAP Nkhoma Synod amakumbukira tsiku lakubadwa kwawo.
Tiyeni tiwafunire zabwino Abusa a Tembo pamene akukondwerera tsiku lakubadwali.