Nyasaland News

Nyasaland News Follow us for well confirmed news, A true non biased Malawian paper,The news that you can trust. htt

24/10/2025

DPP NDI UTM APANGA MGWIRIZANO

Chipani Cha DPP chalowa mumgwirizano ndi chipani cha UTM ku nyumba ya malamuro pofuna kugwilira ntchito limodzi.

Zina mwamfundo za mgwirizanowu ndizakuti aphungu achipani cha DPP akavotere wachiwiri Kwa mtsogoleri wa chipani cha UTM a Dr Catherine Mzumara ngati wachiwiri Kwa spikira wa nyumba ya malamuro.

Mgwirizanowu omweso uli ndi aphungu onse amchigawo cha ku mpoto motsogozedwa ndi Hon Khumbo Kachale, ku UTM motsogozedwa ndi a Dr Patricia Kaliati pamene ku DPP motsogozedwa ndi a Hon Dr Ben Phiri.

Aphungu ambali ziwirizi akhalaso akupanga sapoti Hon Sameer Suleman ngati sipikara oyamba wanyumbayi komanso kugwilira limodzi ngati yokhazikisa ma bill osiyanasiyana.

24/10/2025

Pamudzi pano Nyasaland News yonse ikupita ku holiday, tikumane pa 21 November ya mwezi wa mmawau.

Timakunyadirani Nonse osatira nkhani zathu pano pa nyasaland news.

Nyasaland News
_The News that you can Trust_

24/10/2025

INE SIWACHIWIRI KWA MAYI JANE ANSA KOMA NDINE WACHIWIRI WINA WA PETER MUNTHARIKA_ATERO A ENOCK CHIHANA

2nd Vice President Rt Hon Enoch Chihana wathokoza osatira chipani cha AFORD pokhara odekha kuchokera tsiku lomwe mgwirizano wa Blue Alliance unalowa m'boma kufikira iye atalumbira.

Iye wati Ali ndi chikhulupiliro kuti mgwirizano wawo ndi chipani cha DPP upitilira kuyenda bwino monga momwe ayambira bwino. Iye wati osatira akuyenera kukondana monga momwe akuchitira atsogoleri.

Iwo anatengerapo mwayi odzuzula atolankhani ndi ena omwe akuti iwo ndi "Wachiwiri Kwa Wachiwiri wa mtsogoleri wa dziko" mmalo mwake iwo ati uku ndikulakwitsa chifukwa iwo si wachiwiri Kwa Mayi Jane Ansah koma kwa a Mutharika.

"Ine si Vice President wa Mayi Ansah koma ndine wachiwiri wina wa Mtsogoleri wa dziko lino. Ine ndizipezeka muofesi ya a Mutharika osati mwa a Ansa...munamvapo munthu akakwatira akadzi awiri winayo amakhara mkadzi wa mkadzi oyambayo ?" afunsa a Chihana motero.

23/10/2025

Big shout out to my newest top fans! Francis Hussein, William Chifeni, Frank Ganunkha, Blessings Ng'ona, Cathy Kanyinji, Chireka Hamzy, Alexandre Patricio Taibo, Chisomo Soko, Mathews Nyaika, Chamthondo Solomon, Lovemore Mathambo, Davi Fledson, Olive J Banda, No Nonsense, Evance Chiputi, Timothy Mzis, Ayidah Chikonga, Cindy Small, Samson Gideon, Kondwani Chirwa, Pereya Nicholas, Ishmael Suffy Wadi, Andrew Kho William, Christopher Peter, Chrissy S Sikelo, Adams Khumbodoz, Chance Mwamondwe, Pathy-g Hill, Hastings Chiduza, Richard Chirombo, Omar Ishmail, Justin Jedidiah, Robson Chilinde, Khefa Walelo Mkata, Cosmas Mamu, Doreen Chaima Hulela, Paul Ballack Chinkondenji, Mercy Fundo Perekamoyo, Wiseman Mlowoka Chirwa, Charles Youder Mtanjayani, Michael Daniel, Ngeya Davie, Mada Litso, Alex Gomiwa, Cris Wa Lero Brown, Thomas Ck Thindwa, Josophart Honory Tchika, Lillian Mkwinja, Gift Norman, Zamalad Amin

22/10/2025

UTHENGA SIULEMERA:

Amene muli Mu mzinda wa Johannesburg mdziko la South Africa nkhani ndi imeneyo, akuti musayerekeze kuyala malonda anu mphepete mwa miseu ya mzindau, apopokha nde kununkha linya.

22/10/2025

Abale zikafika apa kujoniko mumatani?

Gulu la anthu kukaronga lazimitsa mnyamata wazaka 17, yemwe dzina lake Francis Msiska, pomupha atazunzidwa kwambiri chif...
22/10/2025

Gulu la anthu kukaronga lazimitsa mnyamata wazaka 17, yemwe dzina lake Francis Msiska, pomupha atazunzidwa kwambiri chifukwa chomuganizira kuti waba nkhuku m'mudzi mwa Mwanganda m'boma lomweli la Karonga.

Padakali pano apolisi m'bomali azuzula gulu la anthuli pokupha mnyamatayu ponena kuti chilango cha wakuba chili kupolisi osati kumudzi.

22/10/2025

Mitu yaima anthu opanda mapepala sakupezekako uku...

Koma izi zachulikira ndithu, atsikana ndi azimayi mdziko muno mungozijambula kanema wa maliseche anu ndikumatumizira amu...
22/10/2025

Koma izi zachulikira ndithu, atsikana ndi azimayi mdziko muno mungozijambula kanema wa maliseche anu ndikumatumizira amuna, kwenikweni chikuchitika ndi chani?

Zili ku coment box ku...

22/10/2025

Kumaberedwa masana Sana pajoni..

22/10/2025

Anyamata inu simukula bwino.

22/10/2025

Mmalawi Otumiza ndalama pa airtel money ku joni kutumizira kumalawi wagwidwa moti akufuna kumupha ataba ndalama zokwanira K3 Million zomwe anapasilidwa kuti atumize koma iye osatumiza mmalo mwake iye ndikuthyolera nthumba mwake ndalamazo kenako ndikuthawa.

Mwamwayi amugwira,akuti mmene amathawamo anathawanso ndi ndalama zambiri za wanthu osiyana siyana omwe amawakopa kuti iye akusintha pamtengo wabwino (rate yokwera bwino).

Address

Opposite Chayamba Building, Along Victoria Avenue Street.
Blantyre
817.9

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Nyasaland News posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Business

Send a message to Nyasaland News:

Share