Nkhani Online

  • Home
  • Nkhani Online

Nkhani Online This is a Non-partizane media house where you can get the true and just coming in news
(1)

01/01/2025

Shout out to my newest followers! Excited to have you onboard! Eric Ej, Tom Nyirongo, Benjamin Peter, Dingiswayo Duncan Gwazayo

08/12/2024



Senior Chief Mwalweni of Rumphi says the rising cases of defilement in his area is due to delay by law enforcers to arrest suspects after reporting.

The Traditional leader was commenting today on reports that his area has recorded at least 21 defilement cases this year alone.

Meanwhile Rumphi District Council Child Protection Worker responsible for this area, Mercy Kalumbi says absence of a court is also fueling the vice.

District Police Spokesperson Sub Inspector Noel Kamchenga has denied that police delay in acting on cases involving children especially defilement cases.

Kamchenga says as police they encourage community members to work hand in hand with them to curb criminal activities.

08/12/2024


Mitengo ya zakumwa monga Fanta komanso Sobo Squash zikwera mtengo kuyambira mawa Lolemba pa 8 December.

Malingana ndi kalata yomwe kampani yopanga zakumwazi ya Coca-Cola Beverages Malawi yatulutsa lero, chakumwa cha Sobo Squash tsopano chidzigulidwa pa K8000 kuchoka pa mtengo wa K6000.

Kalatayi yasonyezanso kuti zakumwa monga Fanta ndi zina zachoka pa 650 botolo lililonse kufika pa K850.

Kampaniyi idakweza mitengo ya zakumwa zake mmwezi wa November chaka chatha kaamba ka kukwera mtengo kwa zipangizo zopangira zakumwazi.

10/10/2024



Nduna yazofalitsa nkhani Moses Kunkuyu watsusa mpheketsera yoti mtsogoleri wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera akudwala.

Polankhula a Kunkuyu ati maripotiwa ndi abodza ndipo boma ligwiritsa ntchito malamulo pothana ndi aliyense yemwe akufalitsa.

Kunkuyu watsindika kuti Dr Chakwera ali mu thanzi labwino ndipo sakudwala choncho anthu apewe kufalitsa zabodzazi.

06/10/2024



Soon after the Tumbuka culture festival Gonapamuhanya ended at Kadumuliro cultural site in Rumphi yesterday, some people were attacked and a minibus carrying people from Phoka had its windows broken.

Police had to fire teargas to control the situation which has left some people injured.

Group Village Headman Chilongozgi of the area has been arrested in connection with the incident and he is at Rumphi police station.

Rumphi Police Station spokesperson, Noel Kamchenga, alleges that the traditional leader was among those who were insulting and pelting stones at people coming from the event.

Kamchenga says police now have the situation under control and security is tight at Bolero.

06/10/2024



Boma lalengeza kuti lero ligawa chimanga cha ulere mmaboma a Thyolo, Mulanje komanso Chikwawa.

Nduna yoona za maboma aang'ono a Richard Chimwendo Banda anena pomwe amalandila president Chakwera pochokera ku America dzulo.

Izi zikuchitika pomwe mdziko lino magwa njala mmadera ambiri.

Padakali pano mwambo wa Mulhako wa Alhomwe, omwe anthu ake ambiri amachokera mmaboma a, Thyolo, Mulanje, Phalombe ndi Zomba ukhala ukuchitika.

A Pious Mvenya ati zomwe zikuchitikazi ndi njira imodzi yoti anthu ambiri asapite ku mwambowu lero koma iwo ati sakutekeseka.

02/10/2024




That's something you don't see everyday!

In the picture is UTM Secretary General Patricia Kaliati, the party's presidential aspirant Newton Kambala, DPP Women's Director Mary Navicha, and Francis Mphepo at the UDF Convention in Blantyre.

Also present is PETRA President Kamuzu Chibambo, Prophet David, and representatives from the People's Party, AFORD, and the National Development Party.

02/10/2024




A Atupele Muluzi afika ku Comesa Hall mu mzinda wa Blantyre kudzakhala nawo pa nsonkhano waukulu wa chipani cha UDF.

Iwo akuyembekezera kutenganso utsogoleri wa chipanichi opanda opikisana naye.

02/10/2024



Former president Dr Bakili Muluzi says the United Democratic Front (UDF) should never be a source of hatred, division and intolerance in the country.

Muluzi says members of the UDF have to learn to live together with all people and promote unity.

The former president was reacting to issues which erupted after the party decided to invite MCP to attend the party's convention.

He said the UDF believes in democracy and that it has been a tradition to call all political parties to attend the national elective conferences.

20/09/2024



Mtsogoleri wa chipani cha UTM Dr Michael Usi ati awonetsesa kuti masomphenya a yemwe anali mtsogoleri wa chipanichi malemu Dr Saulos Klaus Chilima asafe koma apitilire.

Dr Usi ati akudziwa kuti pali anthu ena kuchipani cha UTM omwe akumawanena koma sangayankhe, popereka chitsanzo cha malemba oyera omwe akuti Davide atalowa umfumu panali Asimeye yemwe amamunena koma iye sanayankhe.

A Usi omwenso ndi wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino atsimikizira anthu okhala m'boma la Karonga kuti boma liyesetsa kuti ochita malonda ang'onoang'ono apeze ngongole mosavuta ndikuzitukula pa malonda awo.

20/09/2024



A 32-year-old man identified as Kennedy Ngoma has died after allegedly throwing himself into a moving truck at Jenda in Mzimba.

Jenda police spokesperson Macfarlen Mseteka said the incident occurred on September 19, 2024, at the Jenda-Lilongwe depot, where his relatives were escorting him to Madisi.

Mseteka said it is believed the deceased wanted to relocate to Madisi as he claimed things were not working for him at Jenda.

He alleged that for the past few weeks Ng'oma has been having psychological issues, claiming his life had not turned out the way he had planned it at his age.

As they were waiting for a vehicle at the depot, he threw himself into a moving truck.

20/09/2024



Twelve passengers narrowly escaped unhurt after a Mazda Bongo they were travelling in caught fire in Kasungu last night.

Kasungu Police Deputy spokesperson, Miracle Hauli, says the minibus registration number BR 8537 and the passengers' property have been burned to ashes.

The incident occurred in the Ntondo area along the Kasungu-Lilongwe M1 road from Nkhamenya heading to Lilongwe.

Traffic police officers who stopped the minibus for routine checkups observed fuel droplets from the bottom and alerted the passengers to disembark from the minibus before it caught fire.

Police say inquiries are underway to find out the cause of the incident.

 M'busa wampingo wa Khristu odziwika bwino m'chigawo chakumpoto yemwe amakhala m'boma la Rumphi a Dickson Chivwati Gondw...
20/09/2024


M'busa wampingo wa Khristu odziwika bwino m'chigawo chakumpoto yemwe amakhala m'boma la Rumphi a Dickson Chivwati Gondwe wamwalira.

Akubanja a Austin Gondwe atsimikikiza za imfayi pofotokoza kuti bambo awo amwalilira mu mzinda wa Mzuzu ali ndi zaka 91 atadwala kwa kanthawi.

M'busa Chivwati Gondwe anayamba ntchito ya Ubusa mchaka cha 1967 ndipo wagwira ntchito ndi mamishonale osiyanasiyana kuphatikizapo omwe anabwera mdziko muno kuzakhazikitsa Mpingo wa Khristu.

18/09/2024

The Kasangazi Irrigation Scheme, located in the area of Traditional Authority Kampingo Sibande in Mzimba District, plays a crucial role in the government's initiative for sustainable development in irrigation. This Scheme is designed to revitalise the agricultural sector among smallholder farmers, ensuring they reap the benefits of this project.

Covering a total area of 100 hectares, farmers are currently cultivating 45 hectares at the site. The scheme caters to 300 smallholder farmers, with an active membership of 145 farmers.

The irrigation scheme draws its water supply from the Kasangazi Dam, which was established with funding from the World Bank under the Malawi Drought Recovery and Resilience Project.

This project underscores the government's unwavering commitment to guaranteeing food security for the populace, thereby reducing dependence on rain-fed agriculture in local communities.

18/09/2024



A Yesaya Kaunda, akhalanso m'phunzitsi yemwe wapambana aphunzitsi onse m'boma la Dedza atakhozetsa ana 151 omwe analemba mayeso a sitandade 8 phunziro la masamu ndima A.

Pa ophunzira 155 omwe analemba mayeso a sitandade 8 pa sukulu ya Mantega ku Dedza, ophunzira 151 anakhoza phunziro la masamu ndi ma A pomwe ophunzira anayi okha anakhoza ma B.

Chaka chatha, a Kaunda anakhalanso m'phunzitsi yemwe anakhozetsa ana bwino ku Dedza, atakhozetsa ana phunziro la masamu ma A okwana 130.

Iwo ati, zomwe akupitiliza kuchita zikulimbikitsa ophunzira kumakonda phunziro la masamu tsiku lili lonse komanso kulimbikira maphunziro ngakhale sukulu yawo ili ku mudzi, zikuonetsa phindu lake.

Sukulu ya Mantega yakhalanso sukulu yoyamba pa sukulu 255 za m'bomali

18/09/2024

#

Bungwe la Public Procurement and Disposal of Assets Authority(PPDA) layimitsa ntchito za kampani 8 kaamba kophwanya malamulo oyendetsera ntchito zogula ndi kugulitsa katundu wa boma la PPDA Act (2017).

Kudzera mu kalata imene bungweri latulutsa, kampanizi ndi za Ele Construction, Evic Printing and Stationery Suppliers, Lloyd Auto Parts and General Dealers, Sino Auto and General Dealers, Let's build it, Dallas Stationery and General Supplies, L and C General Dealers Limited ndi Weto Stationery.

Malinga ndi bungweri, Kampanizi sizigwiranso ntchito ndi boma kwa miyezi itatu pomwe zina kufikira zaka zisanu .

"Kampanizi sizololedwa kuchita bizinesi ndi boma mu nthawi yomwe zayimitsidwayi. Nthambi za boma zauzidwa kale za chiganizochi ndipo chikhazikika mpaka nthawi yomwe yaikidwa idzathe kapena pokhapokha patakhala chiletso cha khothi," bungweri latero.

    A Jessie Kabwira agwetsa a Ezekiel Ching'oma pa mpando wa mneneri wa chipanichi ndi mavoti 850 kwa 400.
09/08/2024





A Jessie Kabwira agwetsa a Ezekiel Ching'oma pa mpando wa mneneri wa chipanichi ndi mavoti 850 kwa 400.

09/08/2024





Kumsonkhano wa chipani cha MCP wosankha adindo, zotsatira zosatsimikizika zikuonetsa kuti a Richard Chimwendo Banda ndi omwe apambana pa mpando wa mlembi wa mkulu wa chipani (Secretary General).

Izi ndi malinga zomwe taoona mu chipinda chomwe akuonkhetsera zotsatira, momwe anthu ambiri anayamba kuimba nyimbo zochemelera a Chimwendo Banda, akulu akulu omwe akuyendetsa chisankho atangotsiliza kuwelengetsera zotsatirazi.

Akulu akulu ati alengeza zotsatira akatsiliza kuonkhetsera zonse.

Address


Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Nkhani Online posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Business

Send a message to Nkhani Online:

Videos

Shortcuts

  • Address
  • Telephone
  • Alerts
  • Contact The Business
  • Videos
  • Claim ownership or report listing
  • Want your business to be the top-listed Media Company?

Share