Mtunthama Broadcasting Station

Mtunthama Broadcasting Station Mtunthama Broadcasting Station is a media house broadcasting from Kasungu in Malawi.

The station believes in objectivity, accuracy and creativity throughout it's programming.

 Anthu okwiya amenya komanso kuvulaza mayi Mary Laini Kaude azaka 87 ochokera m'mudzi wa Matewere mdera la mfumu yayikul...
05/01/2025



Anthu okwiya amenya komanso kuvulaza mayi Mary Laini Kaude azaka 87 ochokera m'mudzi wa Matewere mdera la mfumu yayikulu Juma m'boma la Mulanje powaganizira kuti akumanga mvula.

Malinga ndi malipoti anthu ena analowa m'nyumba ya mayiyu ndikuyamba kumumenya ndi cholinga chofuna kumukakamiza kuti amasule mvula.

Anthu ena oyandikira atamva phokoso la anthuwa anathamangira kunyumbayo komwe anawapulumutsa ndikuwatengela ku chipatala chaching'ono cha Namphungo ndipo anawatumiza kuchipatala chachikulu cha bomali komwe anawagoneka kwa masiku awiri akulandira thandizo.

Kutsatira izi bungwe la MANEPO lati ndilokhumudwa ndi nkhaza zomwe anthu achikulire akulandira m'dziko muno.

Kalata yomwe mkulu wa bungweli Andrew Kavala watulutsa yati m'chitidwewu ndikuphwanya ufulu wa anthu achikulire kotero apolisi akuyenera kuchita kafukufuku mwansanga ndikupeza anthu omwe achita izi kuti malamulo agwire ntchito.

Mbali ina ya Kalatayi yapemphanso boma kuteteza kuti likhazikitse ndondomeko za mbwino zomwe zidziteteza ufulu wa anthu achikulire maka a mmadera a kumidzi.

Wolemba Mathews Benard

 Kasungu Police have apprehended Emmanuel Phiri, 26, for allegedly stealing a Maximile motorcycle at Suza Trading Centre...
04/01/2025



Kasungu Police have apprehended Emmanuel Phiri, 26, for allegedly stealing a Maximile motorcycle at Suza Trading Centre. The arrest follows a report by Moses Phiri, a Kabaza operator, who claimed his red motorcycle with engine number 162FMJNJ002477 and chassis number L5DPCJB63NJ002477 went missing on December 19, 2024.

According to Kasungu Deputy Public Relations Officer Sergeant Miracle Hauli, the police acted swiftly upon receiving the complaint. “Through intelligence collection, we managed to trace and arrest the suspect while he was offering the stolen motorcycle for sale. The motorcycle has been positively identified by the complainant,” said Hauli.

Emmanuel Phiri, who hails from Chisi Village, Traditional Authority Tengani in Nsanje District, is currently in custody and will appear in court soon to answer theft charges.

Reported by Mathews Benard

 -OnlineMinistry of Education Delays Opening of Three TTCs Due to Cyclone DamageThe Ministry of Education has announced ...
04/01/2025

-Online

Ministry of Education Delays Opening of Three TTCs Due to Cyclone Damage

The Ministry of Education has announced a delay in the opening of Kasungu, Phalombe, and Chikwakwa Teacher Training Colleges (TTCs) from the initially scheduled date of 6 January 2025 to 20 January 2025.

According to a statement signed by the Secretary for the Ministry, Mangani Katundu, the postponement is due to the impact of Cyclone Chido, which caused significant damage to infrastructure at the three TTCs. Critical structures, including classrooms, kitchens, and hostels, were affected and require repairs to ensure they are safe and functional before the schools reopen.

The ministry has assured the public that efforts are underway to restore the facilities and ensure readiness by the new opening date of 20 January.

Meanwhile, all primary and secondary schools, as well as other TTCs across the country, are expected to resume on 6 January 2025 as planned.

- News- 4- JAN 2025

 Kasungu North Member of Parliament, Mike Bango, has praised the Government of Malawi for its ongoing maize distribution...
03/01/2025



Kasungu North Member of Parliament, Mike Bango, has praised the Government of Malawi for its ongoing maize distribution initiative aimed at supporting vulnerable households.

Speaking at Chisikwa during one of the distribution exercises, Bango urged beneficiaries in his constituency to refrain from selling the maize they receive, emphasizing the importance of using the aid for its intended purpose.

Senior Group Chisikwa echoed these sentiments, assuring that local leaders will ensure all beneficiaries comply and use the maize to address food insecurity.

One of the recipients, Witness Banda, expressed gratitude to the government and President Dr. Lazarus Chakwera for the assistance, stating she would not sell the maize provided to her family.

The maize distribution, coordinated by the Department of Disaster Risk Management Affairs (DoDMA), targets vulnerable households across Malawi. In Kasungu North, 5,014 beneficiaries from areas including Traditional Authorities Chisikwa, Kaluluma, Chisemphere, Kalikokha, and STA Chikwa are expected to benefit from the program.

This initiative underscores the government’s commitment to alleviating food insecurity in the country.

Reported by Linly Kamanga

 Mtsogoleri wadziko lino Dr Lazarus Chakwera wasankha nduna zina za boma  zatsopano.Mwachinsanzo a Ezekiel Peter Ching'o...
01/01/2025



Mtsogoleri wadziko lino Dr Lazarus Chakwera wasankha nduna zina za boma zatsopano.

Mwachinsanzo a Ezekiel Peter Ching'oma asankhidwa kukhala nduna ya chitetezo cha m'dziko kulowa m'malo mwa Ken Zikhale Ng'oma omwe tsopano ndi nduna yoona zamigodi.

Mneneri wachipani Cha Malawi Congress-MCP Jessy Kabwira wasankhidwa kukhala nduna yoona zamaphunziro m'sukulu za ukachenjede.

Ndipo Zina mwa nduna zomwe zasankhidwa kumene ndi yemwe anali wachiwiri kwa nduna ya za maboma aang'ono a Owen Chomanika omwe tsopano ndi nduna za chilengedwe ndi kusintha kwa nyengo.

A Monica Chang'anamuno omwe anali nduna ya za migodi tsopano asankhidwa kukhala nduna ya chitetezo.

Wolemba: Linly Kamanga

 Lilongwe Police Public Relations Officer, Hastings Chigalu, has reported that police at Mitundu recovered a CZ P-09 pis...
01/01/2025



Lilongwe Police Public Relations Officer, Hastings Chigalu, has reported that police at Mitundu recovered a CZ P-09 pistol from unidentified criminals who were allegedly planning to commit a crime at Mkwezalamba Village in Traditional Authority Chiseka on December 31, 2024.

Chigalu stated that around 19:00 hours, officers at Mitundu Police Unit received a tip-off from concerned community members about suspected criminals gathering at a specific location with suspicious motives.

Acting swiftly, the police arrived at the scene, causing the suspects to abandon a plastic bag containing the firearm and flee. The pistol, which was found without ammunition, will be sent to the Fi****ms and Ballistics Department for analysis.

Investigations are ongoing to identify and apprehend the suspects.

Meanwhile, the police have praised the strong partnership between law enforcement and the community, emphasizing how shared information has led to the recovery of stolen property and the arrest of criminal suspects.

Reported by Jacqueline Beauty Chinseu

The management and staff of Mtunthama Broadcasting Station wish you all a Happy and Prosperous New Year.
01/01/2025

The management and staff of Mtunthama Broadcasting Station wish you all a Happy and Prosperous New Year.

Artist wa nthawi zonse, pomwe kwatsala maola ochepa kuti nyimbo yake ilile ponseponse mawu anu ndi otani ?
31/12/2024

Artist wa nthawi zonse, pomwe kwatsala maola ochepa kuti nyimbo yake ilile ponseponse mawu anu ndi otani ?

  Apolisi m'boma la Kasungu amanga  Daniel Paudala yemwe amagwira ntchito  ngati mlonda pa office ya za maphunziro a za ...
30/12/2024



Apolisi m'boma la Kasungu amanga Daniel Paudala yemwe amagwira ntchito ngati mlonda pa office ya za maphunziro a za ulimi ku Lisasadzi pomuganizira kuti adatchyola ofesiyi ndi kuba katundu wa ndalama pafupifupi K5 million.

Wachiwiri kwa mneneri wa polisi m'bomali a Miracle Hauli wati izi zachitika kuyambira usiku wa pakati pa 22 komanso pa 28 mwezi uno.

Malinga ndi Hauli Paudala anapezerapo mwayi pa tchuthi cha khisimasi pomwe anthu anali kunyumba zomwe zidapereka mpata kwa iye kuti kuti atchyole ndi kuba katundu.

Pakanali pano Paudala akusungidwa m'chitokosi cha apolisi ndipo akawonokera ku bwalo la milandu posachedwa komwe mwazina akayankhe mlandu omwe alumuganizira.

Paudala amachokera m'mudzi wa Bondo mfumu yaikulu Kaomba m'bomali.

 Kasungu west Member of Parliament, Jailos Bonongwe, has called for unity and collaboration among politicians, tradition...
29/12/2024



Kasungu west Member of Parliament, Jailos Bonongwe, has called for unity and collaboration among politicians, traditional leaders, community members, and area development committees, emphasizing that such partnerships are vital for driving development in local communities.

Bonongwe made the remarks during the inauguration of a newly constructed bridge at Lisandwa River in the area of Senior Chief Kawamba, Kasungu. The bridge, built at an estimated cost of 35 million Kwacha, was constructed to address challenges faced by residents, especially during the rainy season.

“Even in areas where I may face criticism, I remain committed to serving and supporting the community through impactful development initiatives,” said Bonongwe. He further encouraged leaders to prioritize community needs over political and personal differences.

Senior Chief Kawamba expressed gratitude for the project, highlighting its role in improving safety and accessibility for the local population. The chief also assured that the community would ensure proper maintenance of the bridge to preserve its functionality for years to come.

The completion of the bridge marks a significant step forward for the Kakhome area, enhancing connectivity and improving the livelihoods of the people.

Reported by Jacqueline Beauty Chinseu

29/12/2024

Football match Live

Chulu Football Club Vs Mphomwa FC

29/12/2024

Live now

 Ana a Yahweh Entertainment Presents 2024 Shutdown Urban Muzik ShowUrban music fans in Kasungu are in for a big treat as...
28/12/2024



Ana a Yahweh Entertainment Presents 2024 Shutdown Urban Muzik Show

Urban music fans in Kasungu are in for a big treat as Ana a Yahweh Entertainment hosts the 2024 Shutdown Urban Muzik Show on December 29, 2024, at the Kasungu Community Hall starting at 1 PM.

The event will feature over 30 artists, blending both established names and upcoming talent. It will also include awards in four major categories: Best Urban Male Artist, Best Urban Female Artist, Song of the Year, and Best Urban Producer of the Year.

Noel Nkubwi, founder of Ana a Yahweh Entertainment, says the event is free to attend to ensure it’s accessible to everyone. “This is more than a show—it’s a platform for young artists to showcase their talent and an opportunity to empower the youth through creativity,” he said.

This event builds on the success of the Mother’s Day Show held earlier this year at Chithiba Ground, which received overwhelming support from both fans and artists. Inspired by that success, Ana a Yahweh Entertainment is determined to continue supporting the local creative industry and combating youth unemployment through the arts.

Music lovers and supporters of local talent are encouraged to attend this unforgettable celebration of Malawi’s urban music scene.

Reported by Mathews Benard

 MP Khumbize Chiponda Distributes Maize to 1,200 Households in KasunguMember of Parliament for the south East  constitue...
28/12/2024



MP Khumbize Chiponda Distributes Maize to 1,200 Households in Kasungu

Member of Parliament for the south East constituency in Kasungu District, Khumbize Kandodo Chiponda, has provided maize to 1,200 households in a bid to address hunger affecting several areas in the district.

The distribution took place on Saturday, December 28, 2024, at Chinkhoma school ground in the district.

Speaking during the event, Chiponda criticized the widespread practice of selling farmland and corrupt dealings by some traditional leaders, such as nepotism in village matters.

She described these practices as major contributors to the ongoing food insecurity in the district and called for change.

In his remarks Sub TA Chambwe, commended Chiponda for her intervention, highlighting that the assistance would enable people in his area to focus on their daily activities without the worry of hunger. Chambwe also pledged to enforce a ban on the selling of farmland as a strategy to combat hunger.

One of the beneficiaries, Alinafe Phiri, expressed gratitude to the government for the support, stating that the maize would help sustain her family. However, she appealed for additional help, particularly with fertilizer, to ensure a better harvest in the coming farming season.

The maize distribution covered villages under Chief Chambwe, including Chiwumnya and a few others.

This initiative aims to provide immediate relief to households affected by the food crisis while addressing long-term strategies to mitigate hunger.

Reported by Jacqueline Beauty Chinseu

 Komishonala wa apolisi m'chigawo cha pakati ku m'mawa Rhoda Manjolo wati m'chaka cha 2024 chiwerengero cha abambo omwe ...
27/12/2024



Komishonala wa apolisi m'chigawo cha pakati ku m'mawa Rhoda Manjolo wati m'chaka cha 2024 chiwerengero cha abambo omwe adzipha chakwera kwambiri poyelekeza ndi Chaka chatha.

A Manjolo ati anthu onse omwe adzipha m'chakachi ndi 74 ndipo mwachiwerengelochi 64 ndi amuna ndipo 10 ndi akazi.

Malinga ndi a Manjolo abambo ambiri sayankhula akakhala ndi nkhawa komanso akamakumana ndi mavuto zomwe ati zikukolezera m'chitidwewu.

Kotero Iwo atsimikiza kuti m'chaka cha 2025 awonetsetsa kuti abambo akufikilidwa komanso kuphunzitsidwa kufunikira kogawana nkhawa zawo ndi ena ndi cholinga chofuna kuthana ndi m'chitidwewu.

Izi zayankhulidwa pa phwando lomwe lili nkati ku sukulu ya sekondale ya Loyola m'boma la Kasungu komwe mwazina akukondwelera momwe agwilira ntchito m'chakachi.

Poyankhulapo pa nkhaniyi Osman Gondwe yemwe anayimira mkulu wa apolisi m'dziko muno wapempha anthu kuti asamaope kuwafikira apolisi akhala ndi nkhawa kapena dandaulo.

Phwandoli labweretsa pamodzi apolisi kuchokera m'maboma a Salima, Kasungu , Dowa, Nkhotakota komanso Ntchisi.

Wolemba:Mathews Benard

 Gilbert Moyo, vying for Vice President of the Film Association of Malawi (FAMA), has unveiled plans to establish Kanema...
27/12/2024



Gilbert Moyo, vying for Vice President of the Film Association of Malawi (FAMA), has unveiled plans to establish Kanema House to strengthen the industry. Inspired by the founders of Mtolankhani House, he intends to fundraise for the initiative.

In an interview with Mtunthama Online, Moyo aims to create regional chapters to engage communities in film, offer free workshops for aspiring filmmakers, and implement a mentorship program to connect industry veterans with newcomers. He also plans to address film distribution challenges and foster collaboration between filmmakers and organizations like Cossoma.

With 15 films to his name, including Fatsani and Tsogolo Lathu, Moyo is committed to advancing Malawian cinema.

Moyo revealed this as the Film Association of Malawi prepares to hold its elections on January 5, 2025.

Reported by MAry Chakhaza

26/12/2024

Big shout out to our newest top fans! Ezekiele Ezekiele Banba Blessings Nkhunda Mathew Betha Hosea C Daves Banda Henry Kachigwada Miston Anthony Linly Kamanga Lloyd Banda Jonathan Kamtanthiko Paul Medson Mc Lin Lisimba ISaac Kazira Becky Sembereka Wanangwa Tembo Humphreys Mpasanje George

25/12/2024

The Chairman, Board Members, Management, and Staff of Mtunthama Broadcasting Station wish you all a Merry Christmas and a Prosperous New Year.


Address

Box 125
Kasungu

Opening Hours

09:00 - 17:00

Telephone

+265999017357

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Mtunthama Broadcasting Station posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Business

Send a message to Mtunthama Broadcasting Station:

Videos

Share